Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Onsewo adzasiyidwa kuti mbalame za m’mapiri zodya nyama, ndi nyama zakutchire za padziko lapansi,+ ziwadye. Mbalame zodya nyamazo zidzakhala zikuwadya chilimwe chonse, ndipo nyama zonse zakutchire za padziko lapansi zidzakhala zikuwadya m’nyengo yonse yokolola.+

  • Ezekieli 29:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iwe ndidzakutaya m’chipululu pamodzi ndi nsomba zonse za m’ngalande za Nailo.+ Udzagwera panthaka+ ndipo palibe amene adzakutenge kukakuika m’manda. Ndidzakupereka kwa zilombo zakutchire ndi zolengedwa zouluka kuti ukhale chakudya chawo.+

  • Ezekieli 32:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndidzakusiya pamtunda ndiponso ndidzakuponya kuchigwa.+ Ndidzachititsa kuti zolengedwa zonse zouluka m’mlengalenga zitere pa iwe. Ndidzakhutitsa zilombo zakutchire ndi nyama yako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena