Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 7:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “Nkhani imeneyi yathera pamenepa. Tsopano ineyo Danieli, ndinachita mantha kwambiri moti ndinakhala ngati ndakomoka. Koma nkhaniyi ndinaisunga mumtima mwanga.”+

  • Danieli 8:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ndiyeno ineyo Danieli ndinatopa kwambiri ndipo ndinadwala kwa masiku angapo.+ Kenako ndinadzuka ndi kugwira ntchito yotumikira mfumu.+ Koma ndinali wodabwa kwambiri ndi zimene ndinaona, ndipo palibe amene anazimvetsa.+

  • Habakuku 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nditamva mawu ake, m’mimba mwanga munayamba kubwadamuka ndipo milomo yanga inanjenjemera. Mafupa anga anayamba kuwola+ ndipo ndinanthunthumira chifukwa cha mmene zinthu zinalili. Choncho ndidzayembekezera mofatsa tsiku la nsautso.+ Tsiku limeneli lidzabwera kwa anthu+ ngati mmene munthu amabwerera kwa adani ake kuti awaukire.

  • Mateyu 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ophunzirawo atamva zimenezi, anagwada n’kuwerama mpaka nkhope zawo pansi ndipo anachita mantha kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena