Salimo 111:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chiyambi cha nzeru ndicho kuopa Yehova.+ ש [Sin]Onse otsatira malamulo a Mulungu ndi ozindikira.+ ת [Taw]Iye ayenera kutamandidwa mpaka muyaya.+ Miyambo 3:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ukachita zimenezi, Mulungu ndi anthu adzakukomera mtima ndipo adzakuona kuti ndiwe wozindikira.+ Danieli 11:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Anthu ozindikira+ pakati pa anthuwo adzathandiza anthu ambiri kumvetsa zinthu.+ Iwo adzapunthwa kwa kanthawi ndi lupanga ndi malawi a moto. Adzapunthwanso mwa kutengedwa ukapolo ndi kuwonongedwa kwa zinthu zawo.+ Danieli 12:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “Anthu ozindikira adzawala ngati kuwala kwa kuthambo.+ Ndipo amene akuthandiza anthu ambiri kukhala olungama+ adzawala ngati nyenyezi mpaka kalekale, inde, kwamuyaya. 1 Yohane 5:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anabwera,+ ndipo anatipatsa nzeru+ kuti timudziwe woonayo.+ Ndipo ife ndife ogwirizana+ ndi woonayo, kudzera mwa Mwana wake Yesu Khristu. Iyeyo ndiye Mulungu woona+ ndiponso wopereka moyo wosatha.+
10 Chiyambi cha nzeru ndicho kuopa Yehova.+ ש [Sin]Onse otsatira malamulo a Mulungu ndi ozindikira.+ ת [Taw]Iye ayenera kutamandidwa mpaka muyaya.+
33 Anthu ozindikira+ pakati pa anthuwo adzathandiza anthu ambiri kumvetsa zinthu.+ Iwo adzapunthwa kwa kanthawi ndi lupanga ndi malawi a moto. Adzapunthwanso mwa kutengedwa ukapolo ndi kuwonongedwa kwa zinthu zawo.+
3 “Anthu ozindikira adzawala ngati kuwala kwa kuthambo.+ Ndipo amene akuthandiza anthu ambiri kukhala olungama+ adzawala ngati nyenyezi mpaka kalekale, inde, kwamuyaya.
20 Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anabwera,+ ndipo anatipatsa nzeru+ kuti timudziwe woonayo.+ Ndipo ife ndife ogwirizana+ ndi woonayo, kudzera mwa Mwana wake Yesu Khristu. Iyeyo ndiye Mulungu woona+ ndiponso wopereka moyo wosatha.+