Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iyo inadzitama kwambiri mpaka kukafika kwa Kalonga wa khamulo.+ Inalanda Kalongayu nsembe yoyenera kuperekedwa nthawi zonse,+ ndipo malo opatulika amene iye anakhazikitsa anagwetsedwa.+

  • Danieli 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ndiyeno padzauka magulu ankhondo* otuluka mwa iye. Maguluwo adzaipitsa malo opatulika+ amene ndi malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri, ndipo adzachotsa nsembe zoyenera kuperekedwa nthawi zonse.+

      “Iwo adzaika pamalowo chinthu chonyansa+ chobweretsa chiwonongeko.+

  • Aheberi 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kudzera mwa iye, tiyeni nthawi zonse tizitamanda Mulungu. Tizichita zimenezi monga nsembe imene tikupereka kwa Mulungu,+ yomwe ndi chipatso cha milomo yathu.+ Timagwiritsa ntchito milomo imeneyi polengeza dzina lake kwa anthu ena.+

  • 1 Petulo 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 inunso monga miyala yamoyo mukumangidwa n’kukhala nyumba yauzimu+ kuti mudzakhale ansembe oyera, n’cholinga chakuti mupereke nsembe zauzimu+ zovomerezeka pamaso pa Mulungu kudzera mwa Yesu Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena