Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Andireya, Filipo, Batolomeyo, Mateyu, Tomasi, Yakobo mwana wa Alifeyo, Tadeyo, Simoni Kananiya,*

  • Luka 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye anasankha Simoni, amenenso anam’patsa dzina lakuti Petulo,+ ndi m’bale wake Andireya. Anasankhanso Yakobo ndi Yohane,+ Filipo+ ndi Batolomeyo,

  • Yohane 1:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Kenako Filipo anapeza Natanayeli+ n’kumuuza kuti: “Uja amene Mose analemba za iye m’Chilamulo+ komanso wotchulidwa m’Zolemba za aneneri,+ ife tam’peza. Iyeyu ndi Yesu, mwana wa Yosefe,+ wa ku Nazareti.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena