-
Levitiko 13:49Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
49 ndipo nthendayo ikuoneka yobiriwira mopitira ku chikasu kapena yofiirira pachovala kapena pachikopa, m’litali kapena m’lifupi mwa nsalu, kapena pachinthu chilichonse chopangidwa ndi chikopa, imeneyo ndi nthenda ya khate ndipo iyenera kusonyezedwa kwa wansembe.
-