Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 23:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma khamu lonse linafuulira pamodzi kuti: “Ameneyu muthane naye basi,+ koma ife mutimasulire Baraba!”+

  • Yohane 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma iwo anafuula kuti: “Muthane naye! Muthane naye! M’pachikeni!” Pilato anawafunsa kuti: “Kodi ndipachike mfumu yanu?” Ansembe aakulu anayankha kuti: “Tilibe mfumu ina koma Kaisara.”+

  • Machitidwe 22:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iwo anali kumumvetsera mpaka pa mawu amenewa. Kenako anafuula kuti: “Munthu ameneyu asapezekenso padziko lapansi, chifukwa sakuyenera kukhala ndi moyo!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena