Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 21:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Khamu la anthu linali kuwatsatira, likufuula kuti: “Aphedwe ameneyo!”+

  • Machitidwe 23:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chotero anapita kwa ansembe aakulu+ ndi kwa akulu kukanena kuti: “Ife tachita lumbiro ndi kudzitemberera kuti sitilawa chakudya kufikira titapha Paulo.

  • Machitidwe 25:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndiyeno Fesito ananena kuti: “Mfumu Agiripa ndi anthu nonse amene muli nafe pano, mukumuona munthu uyu. Ayuda onse anandipempha ine ku Yerusalemu komanso kuno, mofuula kuti iyeyu sayeneranso kukhala ndi moyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena