Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 34:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamenepo Yehova anauza Mose kuti: “Dzilembere mawuwa+ chifukwa ine ndikuchita pangano ndi iwe ndi Isiraeli mogwirizana ndi mawu amenewa.”+

  • Deuteronomo 31:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mose atangomaliza kulemba mawu onse a chilamulo ichi m’buku,+

  • 2 Mafumu 23:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno mfumuyo inapita kunyumba ya Yehova pamodzi ndi amuna onse a ku Yuda, anthu onse okhala ku Yerusalemu, ansembe,+ aneneri, ndi anthu onse kuyambira wamng’ono mpaka wamkulu.+ Tsopano mfumuyo inayamba kuwawerengera+ mawu onse a m’buku+ la pangano+ limene linapezeka m’nyumba ya Yehova.+

  • Aefeso 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pakuti iye ndiye mtendere wathu,+ amene analumikiza mbali ziwiri+ kukhala imodzi,+ ndi kugwetsa khoma+ lowalekanitsa limene linali pakati pawo.+

  • Aheberi 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithudi, ndiye kuti malamulo oyambawo akuchotsedwa chifukwa chakuti ndi ofooka+ ndiponso operewera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena