Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 M’patseni Yehova ulemerero wa dzina lake,+

      Tengani mphatso n’kubwera nayo pamaso pake.+

      Gwadirani Yehova mutavala zovala zokongola ndi zopatulika.+

  • Salimo 95:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Bwerani timuweramire ndi kumupembedza.+

      Tiyeni tigwade+ pamaso pa Yehova amene ndiye Wotipanga.+

  • Chivumbulutso 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo ndinagwada pansi n’kuwerama patsogolo pa mapazi ake kuti ndimulambire.+ Koma iye anandiuza kuti:+ “Samala! Usatero ayi! Inetu ndangokhala kapolo mnzako, ndi wa abale ako amene ali ndi ntchito yochitira umboni za Yesu.+ Lambira Mulungu,+ pakuti kuchitira umboni za Yesu ndiko cholinga cha maulosi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena