Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 16
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 16:1

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto 13.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:2; 13:4
  • +Eks 12:14; Le 23:5; Nu 9:2; 28:16; 1Ak 5:7; Ahe 11:28
  • +Eks 34:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Baibulo la Dziko Latsopano (nwt), ptsa. 2136, 2244

Deuteronomo 16:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 26:17; Lu 22:7
  • +Eks 12:5; 2Mb 35:7
  • +De 12:5; 1Mf 8:29

Deuteronomo 16:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:3; Le 23:6; Nu 28:17; 1Ak 5:8
  • +Eks 12:33
  • +Eks 12:14; 13:8, 9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1990, ptsa. 16-17

Deuteronomo 16:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:15; 13:7
  • +Eks 12:10; 34:25

Deuteronomo 16:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 16:2
  • +Eks 12:6; Nu 9:3; Mt 26:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1990, ptsa. 13-14

Deuteronomo 16:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:8; 2Mb 35:13
  • +2Mf 23:23; Yoh 2:13; 11:55

Deuteronomo 16:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:16; Le 23:8

Deuteronomo 16:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:16; 34:22; Le 23:15

Deuteronomo 16:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 28:26; 2Mb 8:13
  • +De 16:17; 1Ak 16:2; 2Ak 8:12

Deuteronomo 16:11

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwana wamwamuna wopanda bambo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:7
  • +Nu 15:16
  • +De 10:18
  • +Yak 1:27
  • +De 12:5

Deuteronomo 16:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 15:13; Eks 3:7; De 5:15
  • +Mla 12:13; 1Yo 5:3

Deuteronomo 16:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:16; Le 23:34; Nu 29:12; De 31:10; Zek 14:16; Yoh 7:2

Deuteronomo 16:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 23:40; De 12:12; 26:11; Ne 8:10, 17; Mla 5:18

Deuteronomo 16:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 23:36; Ne 8:18
  • +De 7:13; 28:8; 30:16
  • +Afi 4:4; 1At 5:16

Deuteronomo 16:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:14; 34:23
  • +Eks 23:15; Le 23:6; Nu 28:17
  • +De 16:10
  • +De 16:13
  • +Eks 23:15; 34:20; Sl 96:8

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    3/2022, ptsa. 22-24

    Nsanja ya Olonda,

    3/1/1998, ptsa. 8-9

    9/15/1995, tsa. 22

Deuteronomo 16:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 16:10; 2Ak 8:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 46

    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira, ptsa. 196-197

Deuteronomo 16:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 18:26; De 1:16; 2Mb 19:5
  • +Nu 11:16; 1Mb 23:4

Deuteronomo 16:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:2; Le 19:15; 1Sa 8:3
  • +De 1:17; Miy 24:23; Mac 10:34
  • +Eks 23:8; 1Sa 12:3; Mla 7:7; Amo 5:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1989, tsa. 12

Deuteronomo 16:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 25:16; Eze 18:8; Mik 6:8
  • +De 4:1

Deuteronomo 16:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:13; Owe 3:7; 2Mb 33:3

Deuteronomo 16:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:24; Le 26:1; De 12:3
  • +De 12:31; Yer 44:4

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 16:1Eks 12:2; 13:4
Deut. 16:1Eks 12:14; Le 23:5; Nu 9:2; 28:16; 1Ak 5:7; Ahe 11:28
Deut. 16:1Eks 34:18
Deut. 16:2Mt 26:17; Lu 22:7
Deut. 16:2Eks 12:5; 2Mb 35:7
Deut. 16:2De 12:5; 1Mf 8:29
Deut. 16:3Eks 13:3; Le 23:6; Nu 28:17; 1Ak 5:8
Deut. 16:3Eks 12:33
Deut. 16:3Eks 12:14; 13:8, 9
Deut. 16:4Eks 12:15; 13:7
Deut. 16:4Eks 12:10; 34:25
Deut. 16:6De 16:2
Deut. 16:6Eks 12:6; Nu 9:3; Mt 26:20
Deut. 16:7Eks 12:8; 2Mb 35:13
Deut. 16:72Mf 23:23; Yoh 2:13; 11:55
Deut. 16:8Eks 12:16; Le 23:8
Deut. 16:9Eks 23:16; 34:22; Le 23:15
Deut. 16:10Nu 28:26; 2Mb 8:13
Deut. 16:10De 16:17; 1Ak 16:2; 2Ak 8:12
Deut. 16:11De 12:7
Deut. 16:11Nu 15:16
Deut. 16:11De 10:18
Deut. 16:11Yak 1:27
Deut. 16:11De 12:5
Deut. 16:12Ge 15:13; Eks 3:7; De 5:15
Deut. 16:12Mla 12:13; 1Yo 5:3
Deut. 16:13Eks 23:16; Le 23:34; Nu 29:12; De 31:10; Zek 14:16; Yoh 7:2
Deut. 16:14Le 23:40; De 12:12; 26:11; Ne 8:10, 17; Mla 5:18
Deut. 16:15Le 23:36; Ne 8:18
Deut. 16:15De 7:13; 28:8; 30:16
Deut. 16:15Afi 4:4; 1At 5:16
Deut. 16:16Eks 23:14; 34:23
Deut. 16:16Eks 23:15; Le 23:6; Nu 28:17
Deut. 16:16De 16:10
Deut. 16:16De 16:13
Deut. 16:16Eks 23:15; 34:20; Sl 96:8
Deut. 16:17De 16:10; 2Ak 8:12
Deut. 16:18Eks 18:26; De 1:16; 2Mb 19:5
Deut. 16:18Nu 11:16; 1Mb 23:4
Deut. 16:19Eks 23:2; Le 19:15; 1Sa 8:3
Deut. 16:19De 1:17; Miy 24:23; Mac 10:34
Deut. 16:19Eks 23:8; 1Sa 12:3; Mla 7:7; Amo 5:12
Deut. 16:20De 25:16; Eze 18:8; Mik 6:8
Deut. 16:20De 4:1
Deut. 16:21Eks 34:13; Owe 3:7; 2Mb 33:3
Deut. 16:22Eks 23:24; Le 26:1; De 12:3
Deut. 16:22De 12:31; Yer 44:4
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 16:1-22

Deuteronomo

16 “Muzisunga mwambo wa m’mwezi wa Abibu*+ pochita chikondwerero cha pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+ 2 Uzipereka nsembe ya pasika kwa Yehova Mulungu wako.+ Uzipereka nkhosa ndi ng’ombe+ pamalo amene Yehova adzasankhe kuikapo dzina lake.+ 3 Usadye nsembeyo pamodzi ndi chilichonse chokhala ndi chofufumitsa. Masiku 7+ uzidya mkate wopanda chofufumitsa, umene ndi mkate wa nsautso, chifukwa unatuluka mofulumira m’dziko la Iguputo.+ Uzichita zimenezi kuti uzikumbukira tsiku limene unatuluka m’dziko la Iguputo, masiku onse a moyo wako.+ 4 Usapezeke ndi mtanda wa ufa wokanda wokhala ndi chofufumitsa m’dziko lako lonse masiku 7.+ Nyama iliyonse imene wapereka nsembe madzulo, pa tsiku loyamba, isagone mpaka m’mawa.+ 5 Sudzaloledwa kupereka nsembe ya pasika mumzinda wanu uliwonse umene Yehova Mulungu wako akukupatsa. 6 Koma uzipereka nsembe ya pasikayo pamalo amene Yehova Mulungu wako adzasankhe kuikapo dzina lake.+ Uzipereka nsembeyo madzulo, dzuwa likangolowa,+ pa nthawi yofanana ndi imene unatuluka mu Iguputo. 7 Uziiwotcha ndi kuidya+ pamalo amene Yehova Mulungu wako adzasankhe,+ ndipo m’mawa mwake uzitembenuka ndi kubwerera kumahema ako. 8 Kwa masiku 6, uzidya mkate wopanda chofufumitsa, ndipo pa tsiku la 7 uzichitira Yehova Mulungu wako+ msonkhano wapadera. Pa tsikuli usagwire ntchito.

9 “Uziwerenga masabata 7. Uziyamba kuwerenga masabata 7 amenewo kuchokera pamene wayamba kumweta tirigu.+ 10 Ndiyeno uzichitira Yehova Mulungu wako+ chikondwerero cha masabata, popereka nsembe zaufulu zimene ungathe, monga mmene Yehova Mulungu wako angakudalitsire.+ 11 Pamenepo uzisangalala pamaso pa Yehova Mulungu wako,+ iweyo, mwana wako wamwamuna, mwana wako wamkazi, kapolo wako wamwamuna, kapolo wako wamkazi, Mlevi wokhala mumzinda wanu, mlendo wokhala pakati panu,+ mwana wamasiye*+ ndi mkazi wamasiye,+ amene ali pakati panu. Muzisangalala pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe kuikapo dzina lake.+ 12 Uzikumbukira kuti unali kapolo ku Iguputo,+ ndipo uzisunga ndi kutsatira malamulo amenewa.+

13 “Uzichita chikondwerero cha misasa+ masiku 7, potuta zokolola kuchokera pamalo opunthira mbewu, pamalo oyengera mafuta ndi pamalo opondera mphesa. 14 Ndipo uzisangalala pa chikondwerero chimenecho,+ iweyo, mwana wako wamwamuna, mwana wako wamkazi, kapolo wako wamwamuna, kapolo wako wamkazi, Mlevi, mlendo wokhala pakati panu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye, amene ali mumzinda wanu. 15 Uzichitira Yehova Mulungu wako chikondwerero chimenecho masiku 7+ pamalo amene Yehova adzasankhe. Uzichita chikondwerero chimenecho chifukwa Yehova Mulungu wako adzakudalitsa+ pa zokolola zako zonse ndi pa chilichonse chimene dzanja lako likuchita, ndipo iwe uzikhala wosangalala basi.+

16 “Mwamuna aliyense pakati panu azikaonekera katatu pa chaka pamaso pa Yehova Mulungu wanu, pamalo amene Mulungu adzasankhe.+ Azikaonekera pa chikondwerero cha mkate wopanda chofufumitsa,+ chikondwerero cha masabata+ ndi pa chikondwerero cha misasa.+ Palibe amene ayenera kuonekera kwa Yehova chimanjamanja.+ 17 Mphatso yochokera m’manja mwa aliyense izikhala yolingana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+

18 “Mudziikire oweruza+ ndi atsogoleri+ m’mizinda yanu yonse imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, malinga ndi mafuko anu. Oweruza ndi atsogoleriwo aziweruza anthu ndi chiweruzo cholungama. 19 Usamapotoze chiweruzo.+ Usamakondere+ kapena kulandira chiphuphu, chifukwa chiphuphu chimachititsa khungu maso a anthu anzeru+ ndi kupotoza mawu a anthu olungama. 20 Uzitsatira chilungamo.+ Ndithudi uzitsatira chilungamo kuti ukhale ndi moyo ndi kukatengadi dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+

21 “Usabzale mtengo wa mtundu uliwonse kuti ukhale mzati woti uziulambira pafupi ndi guwa lansembe la Yehova Mulungu wako limene udzadzipangira.+

22 “Ndipo usadziimikire chipilala chopatulika,+ chinthu chimene Yehova Mulungu wako amadana nacho kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena