Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 8
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 8:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:32; Sl 119:4; 1At 4:1
  • +Miy 3:2
  • +Ge 15:18

Deuteronomo 8:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:7; 29:5; Amo 2:10
  • +Sl 101:5; Lu 18:14; 1Pe 5:6
  • +Eks 16:4; 20:20
  • +De 13:3; Sl 139:23; Miy 17:3

Deuteronomo 8:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:3
  • +Eks 16:31; Sl 78:24
  • +Mt 4:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/2004, ptsa. 13-14

    8/15/1999, ptsa. 25-26

    5/1/1994, tsa. 3

Deuteronomo 8:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:5; Ne 9:21

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/15/2004, tsa. 26

Deuteronomo 8:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 7:14; Miy 3:12; 1Ak 11:32; Ahe 12:6; Chv 3:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/1994, tsa. 3

Deuteronomo 8:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:33; 2Mb 6:31; Sl 128:1; Lu 1:6
  • +1Sa 12:24

Deuteronomo 8:7

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Ge 26:17.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:8; Le 26:4; De 11:12; Ne 9:25
  • +De 11:11

Deuteronomo 8:8

Mawu a M'munsi

  • *

    “Makangaza” ndi mtundu wa chipatso. Ena amati chimanga chachizungu, mwina chifukwa choti njere zake zimaoneka ngati chimanga.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:23
  • +Eze 20:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2011, ptsa. 11-13

    6/15/2006, ptsa. 16-17

    5/15/2000, ptsa. 25, 27

Deuteronomo 8:9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/1/2013, ptsa. 12-13

Deuteronomo 8:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:11
  • +Sl 103:2; 134:1
  • +1Mb 29:14

Deuteronomo 8:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 106:21
  • +De 6:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/1/2006, tsa. 28

    Sukulu ya Utumiki, tsa. 20

Deuteronomo 8:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 32:15; Yer 22:14; Ho 13:6

Deuteronomo 8:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 9:4; 1Ak 4:7
  • +Sl 106:21

Deuteronomo 8:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:19; Yer 2:6
  • +Nu 21:6
  • +Nu 20:11; Sl 78:15; 105:41; 114:8; 1Ak 10:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/1992, tsa. 24

Deuteronomo 8:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:35; Yoh 6:31, 49
  • +De 8:2
  • +2Ak 4:17; Ahe 12:11; 1Pe 1:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/1999, tsa. 25

Deuteronomo 8:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ho 12:8; Hab 1:16; 1Ak 4:7

Deuteronomo 8:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 127:1; Miy 10:22; Ho 2:8
  • +De 7:12

Deuteronomo 8:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:26; 30:18; Yos 23:13; 1Sa 12:25

Deuteronomo 8:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Da 9:11, 12; Amo 3:2

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 8:1De 5:32; Sl 119:4; 1At 4:1
Deut. 8:1Miy 3:2
Deut. 8:1Ge 15:18
Deut. 8:2De 2:7; 29:5; Amo 2:10
Deut. 8:2Sl 101:5; Lu 18:14; 1Pe 5:6
Deut. 8:2Eks 16:4; 20:20
Deut. 8:2De 13:3; Sl 139:23; Miy 17:3
Deut. 8:3Eks 16:3
Deut. 8:3Eks 16:31; Sl 78:24
Deut. 8:3Mt 4:4
Deut. 8:4De 29:5; Ne 9:21
Deut. 8:52Sa 7:14; Miy 3:12; 1Ak 11:32; Ahe 12:6; Chv 3:19
Deut. 8:6De 5:33; 2Mb 6:31; Sl 128:1; Lu 1:6
Deut. 8:61Sa 12:24
Deut. 8:7Eks 3:8; Le 26:4; De 11:12; Ne 9:25
Deut. 8:7De 11:11
Deut. 8:8Nu 13:23
Deut. 8:8Eze 20:6
Deut. 8:10De 6:11
Deut. 8:10Sl 103:2; 134:1
Deut. 8:101Mb 29:14
Deut. 8:11Sl 106:21
Deut. 8:11De 6:12
Deut. 8:12De 32:15; Yer 22:14; Ho 13:6
Deut. 8:14De 9:4; 1Ak 4:7
Deut. 8:14Sl 106:21
Deut. 8:15De 1:19; Yer 2:6
Deut. 8:15Nu 21:6
Deut. 8:15Nu 20:11; Sl 78:15; 105:41; 114:8; 1Ak 10:4
Deut. 8:16Eks 16:35; Yoh 6:31, 49
Deut. 8:16De 8:2
Deut. 8:162Ak 4:17; Ahe 12:11; 1Pe 1:7
Deut. 8:17Ho 12:8; Hab 1:16; 1Ak 4:7
Deut. 8:18Sl 127:1; Miy 10:22; Ho 2:8
Deut. 8:18De 7:12
Deut. 8:19De 4:26; 30:18; Yos 23:13; 1Sa 12:25
Deut. 8:20Da 9:11, 12; Amo 3:2
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 8:1-20

Deuteronomo

8 “Muonetsetse kuti mukusunga lamulo lililonse limene ndikukupatsani lero,+ kuti mupitirize kukhala ndi moyo+ ndi kuti muchulukanedi, n’kupita kukatenga dziko limene Yehova analumbirira makolo anu.+ 2 Muzikumbukira njira yonse imene Yehova Mulungu wanu anakuyendetsani m’chipululu zaka 40 zonsezi.+ Iye anakuyendetsani m’chipululu kuti akuphunzitseni kudzichepetsa,+ kukuyesani+ pofuna kudziwa zimene zinali mumtima mwanu,+ kuti aone ngati mukanasunga malamulo ake kapena ayi. 3 Anakuphunzitsani kudzichepetsa pokukhalitsani ndi njala+ ndi kukudyetsani mana,+ amene inu kapena makolo anu sanawadziwe. Anachita zimenezi kuti mudziwe kuti munthu sakhala ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu onse ochokera m’kamwa mwa Yehova.+ 4 Zovala zanu sizinathe ndipo mapazi anu sanatupe m’zaka 40 zimenezi.+ 5 Inu mukudziwa bwino mumtima mwanu kuti Yehova Mulungu wanu anali kukuwongolerani, ngati mmene bambo amawongolerera mwana wake.+

6 “Muzisunga malamulo a Yehova Mulungu wanu mwa kuyenda m’njira zake+ ndi kumuopa.+ 7 Pakuti Yehova Mulungu wanu akukulowetsani m’dziko labwino,+ dziko la zigwa* za madzi,+ akasupe ndi madzi ochuluka otuluka m’zigwa ndi m’madera a mapiri, 8 dziko la tirigu, balere, mphesa, nkhuyu ndi makangaza,*+ dziko la maolivi opangira mafuta ndiponso la uchi,+ 9 dziko limene mudzadya mkate wosaperewera, limenenso simudzasowa kalikonse, dziko limene miyala yake amapangira zitsulo, limenenso m’mapiri ake mudzakumbamo mkuwa.

10 “Mukadzadya ndi kukhuta+ mudzatamandenso+ Yehova Mulungu wanu, chifukwa cha dziko labwino limene wakupatsani.+ 11 Samalani kuti musaiwale+ Yehova Mulungu wanu ndi kusasunga malamulo, zigamulo ndi mfundo zake zimene ndikukupatsani lero.+ 12 Samalani, kuopera kuti mungadye ndi kukhuta, kumanga nyumba zabwino ndi kukhalamo,+ 13 ng’ombe zanu ndi nkhosa zanu n’kuchuluka, siliva ndi golide wanu n’kuwonjezeka ndiponso zinthu zanu zonse n’kukuchulukirani, 14 mtima wanu n’kuyamba kudzikweza+ ndi kuiwala Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani m’dziko la Iguputo, m’nyumba yaukapolo.+ 15 Mungaiwale amene anakuyendetsani m’chipululu chachikulu ndi chochititsa mantha,+ chokhala ndi njoka zapoizoni,+ zinkhanira ndiponso dziko louma lopanda madzi. Amenenso anakutulutsirani madzi pamwala wolimba ngati nsangalabwi.+ 16 Mungaiwale amene anakudyetsani mana+ m’chipululu, chakudya chimene makolo anu sanachidziwe, pofuna kukuphunzitsani kudzichepetsa+ ndi kuti akuyeseni kuti potsirizira pake akuchitireni zabwino.+ 17 Samalani kuti munganene mumtima mwanu kuti, ‘Chuma ichi ndachipeza ndi mphamvu zanga ndi nyonga za dzanja langa.’+ 18 Muzikumbukira Yehova Mulungu wanu, chifukwa ndiye amakupatsani mphamvu kuti mupeze chuma,+ pofuna kusunga pangano lake limene analumbirira makolo anu, monga mmene wachitira lero.+

19 “Koma mukadzaiwala Yehova Mulungu wanu, n’kutsatira milungu ina, kuitumikira ndiponso kuigwadira, ndikukuchitirani umboni lero kuti anthu inu mudzatha.+ 20 Mudzatheratu ngati mitundu imene Yehova akuiwononga pamaso panu, chifukwa simudzamvera mawu a Yehova Mulungu wanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena