Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 13:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho Abulamu anachoka ku Iguputo nʼkulowera ku Negebu.+ Iye anachoka limodzi ndi mkazi wake ndi zonse zimene anali nazo komanso Loti.

  • Genesis 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Abulamu atachoka ku Negebu, ankamanga misasa malo osiyanasiyana nʼkumasamuka mpaka anakafika ku Beteli, kumene kunali tenti yake poyamba, pakati pa Beteli ndi Ai.+

  • Yoswa 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano Yoswa anatumiza amuna ena kuchokera ku Yeriko kupita ku Ai,+ pafupi ndi Beti-aveni, kumʼmawa kwa Beteli.+ Iye anawauza kuti: “Pitani mukafufuze zokhudza mzindawu.” Amunawo anapita nʼkukafufuza zokhudza mzinda wa Ai.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena