Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 24:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pamene ndinkatulutsa makolo anu ku Iguputo,+ atatsala pangʼono kufika kunyanja, Aiguputo anawathamangira ndi magaleta ankhondo ndiponso amuna okwera pamahatchi, mpaka ku Nyanja Yofiira.+ 7 Iwo anayamba kufuulira Yehova.+ Choncho ndinaika mdima pakati pa iwo ndi Aiguputuwo, ndipo ndinawamiza ndi madzi amʼnyanja.+ Munaona ndi maso anu zimene ndinachita ku Iguputo.+ Kenako inu munakhala mʼchipululu zaka zambiri.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena