Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yehova akuyankheni pa tsiku la mavuto.

      Dzina la Mulungu wa Yakobo likutetezeni.+

  • Salimo 79:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Tithandizeni inu Mulungu amene mumatipulumutsa,+

      Chifukwa cha dzina lanu laulemerero.

      Tipulumutseni komanso mutikhululukire* machimo athu chifukwa cha dzina lanu.+

  • Miyambo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba.+

      Wolungama amathawira mmenemo ndipo amatetezedwa.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena