Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 33:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndi amene amayenda mʼchilungamo nthawi zonse,+

      Amene amalankhula zoona,+

      Amene amakana kupeza phindu pochita zinthu mosaona mtima komanso mwachinyengo,

      Amene manja ake amakana chiphuphu, mʼmalo mochilandira,+

      Amene amatseka makutu ake kuti asamve nkhani zokhudza kukhetsa magazi,

      Ndiponso amene amatseka maso ake kuti asaone zinthu zoipa.

      16 Iye adzakhala pamalo okwera.

      Malo ake othawirako otetezeka* adzakhala mʼmatanthwe movuta kufikamo.

      Iye adzapatsidwa chakudya

      Ndipo madzi ake sadzatha.”+

  • Machitidwe 10:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Petulo atamva zimenezi, anayamba kulankhula kuti: “Ndazindikira ndithu kuti Mulungu alibe tsankho.+ 35 Iye amalandira munthu wochokera mu mtundu uliwonse, amene amamuopa ndi kuchita chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena