Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Muimbireni nyimbo yatsopano.+

      Imbani mwaluso choimbira cha zingwe ndipo muzifuula mosangalala.

  • Salimo 40:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kenako anaika nyimbo yatsopano mʼkamwa mwanga,+

      Nyimbo yotamanda Mulungu wathu.

      Ambiri adzaona zimenezi ndipo adzachita mantha,

      Nʼkuyamba kukhulupirira Yehova.

  • Salimo 98:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 98 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,+

      Chifukwa wachita zinthu zodabwitsa.+

      Dzanja lake lamanja, mkono wake woyera, wabweretsa chipulumutso.*+

  • Salimo 149:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 149 Tamandani Ya!*

      Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,+

      Mutamandeni mumpingo wa anthu ake okhulupirika.+

  • Yesaya 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano.+

      Mʼtamandeni kuchokera kumalekezero a dziko lapansi,+

      Inu nonse amene mumadalira nyanja komanso zonse zimene zimakhala mmenemo,

      Inu zilumba ndi anthu amene amakhala mʼzilumbazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena