Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 100:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Dziwani* kuti Yehova ndi Mulungu.+

      Iye ndi amene anatipanga, ndipo ndife ake.+

      Ndife anthu ake komanso nkhosa zimene akuweta.+

  • Yesaya 54:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa Wokupanga Wamkulu+ ali ngati mwamuna* wako,+

      Dzina lake ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,

      Ndipo Woyera wa Isiraeli ndiye Wokuwombola.+

      Iye adzatchedwa Mulungu wa dziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena