Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndidziwitseni njira zanu, inu Yehova.+

      Ndiphunzitseni kuyenda mʼnjira zanu.+

  • Salimo 86:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndilangizeni inu Yehova, za njira yanu.+

      Kuti ndiyende mʼchoonadi chanu.+

      Ndithandizeni kuti ndiziopa dzina lanu ndi mtima wonse.*+

  • Yesaya 30:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngakhale kuti Yehova adzakupatsani mavuto kuti akhale chakudya chanu ndi kuponderezedwa kuti kukhale madzi anu akumwa,+ Mlangizi wanu wamkulu adzasiya kudzibisa ndipo maso anu adzaona Mlangizi wanu wamkulu.+

  • Yesaya 54:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana ako onse azidzaphunzitsidwa ndi Yehova,+

      Ndipo mtendere wa ana ako udzakhala wochuluka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena