Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndidziwitseni njira zanu, inu Yehova.+

      Ndiphunzitseni kuyenda mʼnjira zanu.+

      ה [He]

       5 Ndithandizeni kuti ndiziyenda mʼchoonadi chanu ndipo mundiphunzitse,+

      Chifukwa inu ndinu Mulungu amene mumandipulumutsa.

      ו [Waw]

      Ndimayembekezera inu tsiku lonse.

  • Salimo 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndilangizeni, inu Yehova, kuti ndiyende mʼnjira yanu.+

      Nditsogolereni mʼnjira yoyenera kuti nditetezeke kwa adani anga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena