Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Musankhe moyo pokonda Yehova Mulungu wanu,+ kumvera mawu ake ndi kukhala okhulupirika kwa iye,+ chifukwa iye ndi amene amapereka moyo ndipo angakuthandizeni kuti mukhale ndi moyo kwa nthawi yaitali mʼdziko limene Yehova analumbira kuti adzalipereka kwa makolo anu, Abulahamu, Isaki ndi Yakobo.”+

  • Salimo 37:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Chifukwa anthu oipa adzaphedwa,+

      Koma amene akuyembekezera Yehova adzalandira dziko lapansi.+

  • Miyambo 2:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa owongoka mtima okha ndi amene adzakhale padziko lapansi,

      Ndipo opanda cholakwa* ndi amene adzatsalemo.+

  • Mateyu 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Osangalala ndi anthu ofatsa+ chifukwa adzalandira dziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena