Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 97:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu amene mumakonda Yehova, muzidana ndi zoipa.+

      Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+

      Amawapulumutsa mʼmanja mwa* oipa.+

  • Miyambo 2:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu owongoka mtima, amawasungira nzeru zopindulitsa.

      Iye ndi chishango kwa anthu amene amachita zinthu mokhulupirika.+

       8 Amayangʼanira njira za anthu amene amachita zachilungamo,

      Ndipo adzateteza njira ya anthu ake okhulupirika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena