Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ‘Yehova ndi wosakwiya msanga, ndiponso wachikondi chokhulupirika chochuluka.*+ Amakhululukira zolakwa ndi machimo, koma sadzalekerera wolakwa osamupatsa chilango. Amalanga ana, zidzukulu ndi ana a zidzukuluzo chifukwa cha zolakwa za abambo awo.’+

  • Salimo 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Musakumbukire machimo amene ndinachita ndili mnyamata komanso zolakwa zanga.

      Mundikumbukire chifukwa cha ubwino wanu, inu Yehova,+

      Mogwirizana ndi chikondi chanu chokhulupirika.+

  • Salimo 41:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ine ndinati: “Inu Yehova, ndikomereni mtima.+

      Ndichiritseni,+ chifukwa ndakuchimwirani.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena