Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 103:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mofanana ndi bambo amene amasonyeza chifundo kwa ana ake,

      Yehova wasonyezanso chifundo kwa anthu amene amamuopa.+

  • Miyambo 28:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Wobisa machimo ake zinthu sizidzamuyendera bwino,+

      Koma amene amawaulula nʼkuwasiya adzachitiridwa chifundo.+

  • Yesaya 43:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ineyo ndi amene ndikufafaniza zolakwa zako*+ chifukwa cha dzina langa,+

      Ndipo machimo ako sindidzawakumbukira.+

  • Yesaya 44:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndidzafafaniza zolakwa zako ndipo zidzakhala ngati ndaziphimba ndi mtambo+

      Ndipo machimo ako adzakhala ngati ndawaphimba ndi mtambo waukulu.

      Bwerera kwa ine, ndipo ine ndidzakuwombola.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena