Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Aliyense wa inu azilemekeza* mayi ndi bambo ake,+ ndipo muzisunga masabata anga.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

  • Miyambo 31:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Amatsegula pakamwa pake mwanzeru,+

      Ndipo lamulo la kukoma mtima lili* palilime lake.

  • 2 Timoteyo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chifukwa ndikukumbukira chikhulupiriro chako chopanda chinyengo,+ chimene anayamba kukhala nacho ndi agogo ako aakazi a Loisi komanso amayi ako a Yunike, ndipo ndikukhulupirira kuti iwenso uli nacho.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena