Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 11:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Sizidzavulazana+

      Kapena kuwonongana mʼphiri langa lonse loyera,+

      Chifukwa dziko lapansi lidzadzaza ndi anthu odziwa Yehova

      Ngati mmene madzi amadzazira mʼnyanja.+

  • Yesaya 65:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mmbulu ndi mwana wa nkhosa zidzadyera pamodzi,

      Mkango udzadya udzu ngati ngʼombe yamphongo,+

      Ndipo chakudya cha njoka chidzakhala fumbi.

      Zimenezi sizidzapweteka aliyense kapena kuwononga chilichonse mʼphiri langa lonse loyera,”+ akutero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena