Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 57:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Amene mukukhala ndi chilakolako champhamvu chogonana pakati pa mitengo ikuluikulu,+

      Pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri?+

      Kodi si inu amene mumapha ana mʼzigwa,*+

      Pakati pa matanthwe?

       6 Gawo lako lili pamodzi ndi miyala yosalala yamʼchigwa.*+

      Inde, gawo lako ndi limeneli.

      Ndipo umapereka nsembe zachakumwa, ndiponso mphatso kwa zinthu zimenezi.+

      Kodi ine ndikhutire* ndi zinthu zimenezi?

  • Yeremiya 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iwo amauza mtengo kuti, ‘Ndinu bambo anga,’+

      Ndipo mwala amauuza kuti, ‘Ndinu amene munandibereka.’

      Koma ine andifulatira ndipo sanandisonyeze nkhope yawo.+

      Koma tsoka likadzawagwera adzanena kuti,

      ‘Bwerani mudzatipulumutse!’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena