Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Davide anawonjezera kuti: “Yehova amene anandipulumutsa mʼkamwa mwa mkango ndi mʼkamwa mwa chimbalangondo andipulumutsanso mʼmanja mwa Mfilisiti ameneyu.”+ Sauli anauza Davide kuti: “Pita, ndipo Yehova akhale nawe.”

  • Aheberi 11:32, 33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kodi ndiperekenso zitsanzo zina? Nthawi indichepera kuti ndipitirize kufotokoza za Gidiyoni,+ Baraki,+ Samisoni,+ Yefita,+ Davide+ komanso Samueli+ ndi aneneri ena. 33 Chifukwa cha chikhulupiriro, anthu amenewa anagonjetsa maufumu pankhondo,+ anachita chilungamo, analonjezedwa zinthu zina+ ndiponso anatseka mikango pakamwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena