Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 4:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Inu munaona mtengo umene unakula kwambiri ndipo unakhala wamphamvu. Nsonga ya mtengowo inakafika mpaka kumwamba ndipo unkaoneka padziko lonse lapansi.+ 21 Masamba ake anali okongola ndipo unali ndi zipatso zambiri. Mumtengomo munali zakudya zokwanira anthu ndi nyama zonse. Nyama zakutchire zinkakhala pansi pake ndipo mbalame zamumlengalenga zinkakhala munthambi zake.+ 22 Mtengowo ndi inuyo mfumu, chifukwa mwakula ndipo mwakhala wamphamvu. Ulemerero wanu wakula mpaka kukafika kumwamba+ ndipo ulamuliro wanu wafika kumalekezero a dziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena