Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 6:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndinu osangalala anthu akamadana nanu,+ kukusalani,+ kukunyozani komanso kukana* dzina lanu nʼkumanena kuti ndi loipa, chifukwa cha Mwana wa munthu. 23 Sangalalani pa tsiku limenelo ndipo mudumphedumphe mokondwera, chifukwa mphoto imene Mulungu adzakupatseni ndi yaikulu,* popeza zinthu zimenezo ndi zimenenso makolo awo akale anachitira aneneri.+

  • Yakobo 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Abale anga, muzisangalala kwambiri pamene mukukumana ndi mayesero osiyanasiyana,+

  • 1 Petulo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndinu osangalala*+ ngati anthu akukunyozani chifukwa cha dzina la Khristu chifukwa zimenezi zikusonyeza kuti mzimu woyera wa Mulungu komanso ulemerero wake zili pa inu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena