Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndifotokoza zimene Yehova wanena.

      Iye wandiuza kuti: “Iwe ndiwe mwana wanga,+

      Lero, ine ndakhala bambo ako.+

  • Mateyu 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Panamvekanso mawu ochokera kumwamba+ onena kuti: “Uyu ndi Mwana wanga+ wokondedwa ndipo amandisangalatsa kwambiri.”+

  • Luka 3:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 ndipo mzimu woyera wooneka ngati nkhunda unatsika kudzamutera. Ndiyeno panamveka mawu ochokera kumwamba akuti: “Iwe ndi Mwana wanga wokondedwa, umandisangalatsa kwambiri.”+

  • 2 Petulo 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chifukwa Khristu analandira ulemu ndi ulemerero kuchokera kwa Mulungu, Atate wathu, pamene mawu anamveka kwa iye kuchokera mu ulemerero waukulu kuti: “Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa, amene amandisangalatsa kwambiri.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena