Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndifotokoza zimene Yehova wanena.

      Iye wandiuza kuti: “Iwe ndiwe mwana wanga,+

      Lero, ine ndakhala bambo ako.+

  • Mateyu 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Patapita masiku 6, Yesu anatenga Petulo, Yakobo ndi mchimwene wake Yohane nʼkukwera nawo mʼphiri lalitali kwaokhaokha.+

  • Mateyu 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mawu ake adakali mʼkamwa, mtambo wowala kwambiri unawaphimba ndipo panamveka mawu kuchokera mumtambomo akuti: “Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa, amene amandisangalatsa kwambiri.+ Muzimumvera.”+

  • Maliko 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno kunachita mtambo umene unawaphimba. Kenako panamveka mawu+ kuchokera mumtambomo akuti: “Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa.+ Muzimumvera.”+

  • Luka 9:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndiyeno panamveka mawu+ kuchokera mumtambomo akuti: “Uyu ndi Mwana wanga, amene ndinamusankha.+ Muzimumvera.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena