Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno mfumuyo inauza mneneri Natani+ kuti: “Ine ndikukhala mʼnyumba ya mitengo ya mkungudza,+ pamene Likasa la Mulungu woona likukhala mutenti.”+

  • 1 Mbiri 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Davide anauza mwana wake Solomo kuti: “Ineyo ndinkafunitsitsa kumanga nyumba ya dzina la Yehova Mulungu wanga.+

  • Salimo 132:1-5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 132 Inu Yehova, kumbukirani Davide

      Komanso mavuto onse amene anakumana nawo.+

       2 Kumbukirani kuti analumbira kwa inu Yehova,

      Analonjeza kwa Wamphamvu wa Yakobo kuti:+

       3 “Sindidzalowa mutenti yanga, mʼnyumba yanga.+

      Sindidzagona pabedi langa.

       4 Sindidzalola kuti ndigone

      Kapena kutseka maso anga,

       5 Mpaka nditamupezera Yehova malo okhala,

      Malo abwino oti* Wamphamvu wa Yakobo azikhalamo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena