Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo andikwiyitsa* ndi milungu yabodza.+

      Andikhumudwitsa ndi mafano awo opanda pake.+

      Choncho ine ndiwachititsa nsanje ndi anthu opanda pake,+

      Ndiwakhumudwitsa ndi mtundu wopusa.+

  • Aroma 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Komanso ndifunse kuti, Kodi si zoona kuti Aisiraeli anadziwa?+ Choyamba Mose anati: “Ndidzakuchititsani nsanje pogwiritsa ntchito anthu omwe si Aisiraeli. Ndidzakukwiyitsani koopsa pogwiritsa ntchito mtundu wopusa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena