Mlaliki 12:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndi zimene munthu akuyenera kuchita.+ Yeremiya 7:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Koma ndinawalamula kuti: “Muzimvera mawu anga, ndipo ndidzakhala Mulungu wanu, inuyo mudzakhala anthu anga.+ Muziyenda mʼnjira imene ndakulamulani, kuti zinthu zikuyendereni bwino.”’+ Aroma 2:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Mdulidwe+ ndi waphindu pokhapokha ngati iweyo umatsatiradi Chilamulo.+ Koma ngati umaphwanya Chilamulo, mdulidwe wako ndi wopanda ntchito. Agalatiya 5:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Chifukwa ngati munthu ali wogwirizana ndi Khristu Yesu, kudulidwa kapena kusadulidwa kumakhala kopanda ntchito.+ Koma chofunika kwambiri nʼkukhala ndi chikhulupiriro chimene chimaonekera posonyeza chikondi. 1 Yohane 5:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Kukonda Mulungu kumatanthauza kutsatira malamulo ake,+ ndipo malamulo akewo si ovuta kuwatsatira.+
13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndi zimene munthu akuyenera kuchita.+
23 Koma ndinawalamula kuti: “Muzimvera mawu anga, ndipo ndidzakhala Mulungu wanu, inuyo mudzakhala anthu anga.+ Muziyenda mʼnjira imene ndakulamulani, kuti zinthu zikuyendereni bwino.”’+
25 Mdulidwe+ ndi waphindu pokhapokha ngati iweyo umatsatiradi Chilamulo.+ Koma ngati umaphwanya Chilamulo, mdulidwe wako ndi wopanda ntchito.
6 Chifukwa ngati munthu ali wogwirizana ndi Khristu Yesu, kudulidwa kapena kusadulidwa kumakhala kopanda ntchito.+ Koma chofunika kwambiri nʼkukhala ndi chikhulupiriro chimene chimaonekera posonyeza chikondi.