Miyambo 28:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Wosangalala ndi munthu amene nthawi zonse amasamala zochita zake,*Koma amene amaumitsa mtima wake adzakumana ndi tsoka.+ Luka 22:33, 34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Kenako iye anauza Yesu kuti: “Ambuye, ndine wokonzeka kupita nanu limodzi kundende kapena kufa nanu limodzi.”+ 34 Koma iye anati: “Ndikukuuza iwe Petulo, tambala asanalire lero, undikana katatu kuti sukundidziwa.”+ Agalatiya 6:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Abale, ngati munthu wapatuka nʼkuyamba kulowera njira yolakwika mosazindikira, inu amene ndi oyenerera mwauzimu, yesani kuthandiza munthu woteroyo ndi mzimu wofatsa.+ Koma pamene mukuchita zimenezi musamale,+ kuopera kuti inunso mungayesedwe.+
14 Wosangalala ndi munthu amene nthawi zonse amasamala zochita zake,*Koma amene amaumitsa mtima wake adzakumana ndi tsoka.+
33 Kenako iye anauza Yesu kuti: “Ambuye, ndine wokonzeka kupita nanu limodzi kundende kapena kufa nanu limodzi.”+ 34 Koma iye anati: “Ndikukuuza iwe Petulo, tambala asanalire lero, undikana katatu kuti sukundidziwa.”+
6 Abale, ngati munthu wapatuka nʼkuyamba kulowera njira yolakwika mosazindikira, inu amene ndi oyenerera mwauzimu, yesani kuthandiza munthu woteroyo ndi mzimu wofatsa.+ Koma pamene mukuchita zimenezi musamale,+ kuopera kuti inunso mungayesedwe.+