Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa kuzungulira anthu onse amene amaopa Mulungu,+

      Ndipo amawapulumutsa.+

  • Salimo 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mavuto* a munthu wolungama ndi ambiri,+

      Koma Yehova amamupulumutsa ku mavuto onsewo.+

  • 2 Timoteyo 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ambuye adzandipulumutsa ku choipa chilichonse ndipo adzandisunga kuti ndikakhale mu Ufumu wake wakumwamba.+ Iye apatsidwe ulemerero mpaka muyaya. Ame.

  • 2 Petulo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Zimenezi zikusonyeza kuti Yehova* amadziwa kupulumutsa anthu odzipereka kwa iye akakhala pa mayesero.+ Koma anthu osalungama amawasunga kuti adzawawononge pa tsiku lopereka chiweruzo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena