Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

FEBRUARY 27, 2012–MARCH 4, 2012

Akhristu Oona Amalemekeza Mawu a Mulungu

TSAMBA 4 • NYIMBO: 113, 116

MARCH 5-11, 2012

Phunzirani Kukhala Maso Kuchokera kwa Atumwi a Yesu

TSAMBA 9 • NYIMBO: 125, 43

MARCH 12-18, 2012

Phunzirani Kuchokera ku Choonadi cha M’chilamulo

TSAMBA 16 • NYIMBO: 107, 13

MARCH 19-25, 2012

Tizipereka Nsembe kwa Yehova ndi Moyo Wathu Wonse

TSAMBA 21 • NYIMBO: 66, 56

MARCH 26, 2012–APRIL 1, 2012

Ansembe Achifumu Amene Adzapindulitse Anthu Onse

TSAMBA 26 • NYIMBO: 60, 102

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 4-8

Nkhaniyi ikusonyeza kuti kuyambira kalekale Akhristu oona akhala akuyesetsa kuti azitsogoleredwa ndi Mawu a Mulungu. Tionanso m’nkhaniyi lemba lathu la chaka cha 2012.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 9-13

Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zitatu zimene tingaphunzire kuchokera kwa atumwi ndiponso Akhristu ena oyambirira pa nkhani ya kukhala maso. Itithandiza kukhala ofunitsitsa kuchitira umboni mokwanira za Ufumu wa Mulungu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 16-25

Chilamulo cha Mose chinkalamula kuti Aisiraeli azipereka nsembe kwa Yehova pa nthawi zosiyanasiyana. Akhristu sayenera kutsatira Chilamulochi. Koma angaphunzire zambiri m’Chilamulochi pa nkhani ya mtima woyamikira womwe Yehova amafuna kuti anthu ake azikhala nawo pomulambira. Nkhanizi zikufotokoza zimenezi.

NKHANI YOPHUNZIRA 5 TSAMBA 26-30

Zimene anthu akufunika kwambiri ndi kugwirizanitsidwa ndi Mulungu. Nkhaniyi ikufotokoza mmene ansembe achifumu adzathandizire kuti zimenezi zitheke. Ikufotokozanso madalitso amene ifeyo tidzapeza.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Zimene Zasintha M’magazini Yophunzira

14 ‘Kodi Mmene Ndililimu Ndingakwanitse Kulalikira?’

15 Zomwe Mungachite Kuti Muzipindula Ndiponso Kusangalala Mukamaphunzira Baibulo

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Banja limene likuchita upainiya ndiponso limene laphunzira chinenero cha Tzotzil likulalikira kwa banja lolankhula chinenerocho. Ali kumsika wa mumzinda wa San Cristóbal de las Casas, ku Mexico.

MEXICO

KULI ANTHU OKWANA

108,782,804

KULI OFALITSA OKWANA

710,454

ZINENERO ZIMENE AMAZIMASULIRA

Zinenero 30 za kumeneko

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena