Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 12/15 tsamba 32
  • Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2014

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2014
  • Nsanja ya Olonda—2014
Nsanja ya Olonda—2014
w14 12/15 tsamba 32

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2014

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

BAIBULO

  • Kodi Linalembedwa Bwanji? 2/1

  • Kodi Luka Analemba Zolondola? 1/1

  • Kodi Ndi Mawudi a Mulungu? 2/1

  • Linafika ku Spain, 3/1

  • Lotchedwa Peshitta, 9/1

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

  • Ankagwiritsa Ntchito Baibulo Poyankha Funso Lililonse (I. Lamela), 4/1

  • Lonjezo la Paradaiso Linasintha Moyo (I. Vigulis), 2/1

  • Ndinali Wodzikonda Kwambiri (C. Bauer), 10/1

  • Ndinkamenya Nkhondo Yolimbana ndi Kupanda Chilungamo Komanso Chiwawa (A. Touma), 8/1

  • Ndinkayenda ndi Mfuti Kulikonse (A. Lugarà), 7/1

  • Yehova Sanandiiwale (S. Udías), 1/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA

  • Ayuda ‘anali kuyembekezera Mesiya’ (Luka 3:15), 2/15

  • Kodi akulu ndi atumiki amaikidwa bwanji? 11/15

  • Kodi n’zoyenera kuti Akhristu azitentha mtembo? 6/15

  • Kodi oukitsidwa padzikoli sadzakwatira kapena kukwatiwa? (Luka 20:34-36), 8/15

  • Kodi Yehova sadzalola kuti Mkhristu avutike ndi njala? (Sal. 37:25; Mat. 6:33), 9/15

  • Mboni ziwiri (Chiv. 11:3-12), 11/15

  • Rakele akulirira ana ake (Yer. 31:15), 12/15

MBIRI YA MOYO WANGA

  • Bambo Anamwalira Koma Ndinapeza Bambo Ena (G. Lösch), 7/15

  • Kutumikira Mulungu Kwandithandiza Kuti Ndikhale Wosangalala (P. Carrbello), 9/1

  • Madalitso mu Utumiki wa Nthawi Zonse (R. Wallen), 4/15

  • Mavuto Andithandiza Kulimbitsa Ubwenzi ndi Yehova (M. Morlans), 3/1

  • Yehova Wandithandiza (K. Little), 5/15

  • Zinthu Zosaiwalika pa Utumiki Wanga (M. Olson), 10/15

MBONI ZA YEHOVA

  • Anadzipereka ku Micronesia, 7/15

  • Anadzipereka ku Taiwan, 10/15

  • Anadzipereka Kumadzulo kwa Africa, 1/15

  • ‘Ankadziwa Njira Yake’ (G. Pierce), 12/15

  • Kodi Amakhulupirira Yesu? 5/1

  • “Ntchito Yokolola Idakalipo” (Brazil), 5/15

  • Padutsa Zaka 100 (Sewero la Pakanema), 2/15

  • Sewero la Eureka, 8/15

  • Uthenga Wabwino ku Japan, 11/15

  • Zimene Ndinasankha Ndili Mwana, 1/15

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

  • Achibale Omwe Si Mboni, 3/15

  • Anthu Opereka ndi Mtima Wonse, 12/15

  • ‘Chakudya N’kuchita Chifuniro cha Mulungu,’ 5/15

  • “Inde Kenako Ayi,” 3/15

  • Kodi Kupemphera N’kothandizadi? 4/1

  • Kodi ‘Mukuyesetsa Kuti Mukhale Woyang’anira’? 9/15

  • Kodi Ndi Bwino Kusintha Maganizo? 12/15

  • Kukana Mayesero, 4/1

  • Kulambira kwa Pabanja, 3/15

  • Mukulandira “Chakudya pa Nthawi Yoyenera,” 8/15

  • ‘Salaza Njira’ Kuti Uyende Bwino, 6/15

  • Tingathandize Akhristu Amene Banja Latha, 6/15

  • ‘Ubwerere Ukalimbikitse Abale Ako,’ 8/15

NKHANI ZOPHUNZIRA

  • Achinyamata Muzisankha Zochita Mwanzeru, 1/15

  • Akazi Amathandiza Pokwaniritsa Cholinga cha Yehova, 8/15

  • Anthu a Yehova Amakana Kuchita Zosalungama, 7/15

  • “Anthu Amene Mulungu Wawo Ndi Yehova,” 11/15

  • “Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba,” 10/15

  • “Inu Ndinu Mboni Zanga,” 7/15

  • Kodi Achikulire Tingawasamalire Bwanji? 3/15

  • Kodi Kuuka kwa Yesu Kumatithandiza Bwanji? 11/15

  • Kodi ‘Mukuona Wosaonekayo’? 4/15

  • Kodi Mukuyenda Limodzi ndi Gulu la Yehova? 5/15

  • Kodi Mumaona Anthu Ofooka Mmene Yehova Amawaonera? 6/15

  • Kodi Mumayamikira Mwayi Wogwira Ntchito ndi Yehova? 10/15

  • Kodi Mumayamikira Zimene Muli Nazo? 12/15

  • Kodi Timamvetsa Tanthauzo Lake? 12/15

  • Kodi Tingatani Kuti Tikhalebe Osangalala? 3/15

  • Kodi ‘Tingayankhe Bwanji Aliyense’? 5/15

  • Kodi Ufumu Umene Walamulira Zaka 100 Umakukhudzani Bwanji? 1/15

  • Kodi Ufumu wa Mulungu Ubwera Liti? 1/15

  • Lambirani Yehova, Mfumu ya Muyaya, 1/15

  • Limbani Mtima, Yehova Akuthandizani, 4/15

  • Makolo, Muzisamalira Bwino Ana Anu, 9/15

  • Mdani Wathu Womalizira Adzawonongedwa, 9/15

  • “Mudzakhala Mboni Zanga,” 7/15

  • ‘Mudzakhala Ufumu wa Ansembe,’ 10/15

  • Muzichitira Anthu Zimene Mungafune Kuti Akuchitireni, 5/15

  • Muzigwiritsa Ntchito Mawu a Mulungu Chifukwa Ndi Amoyo, 8/15

  • Muzikumbukira Atumiki a Nthawi Zonse, 9/15

  • Muzilemekeza Anthu Achikulire, 3/15

  • Muzimva Mawu a Yehova Nthawi Zonse, 8/15

  • ‘Mverani Ndipo Mumvetse Tanthauzo Lake,’ 12/15

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kukhala Oyera? 11/15

  • N’chiyani Chimakutsimikizirani Kuti Muli M’gulu la Yehova? 9/15

  • Sangalalani Chifukwa cha Ukwati wa Mwanawankhosa, 2/15

  • Simungatumikire Ambuye Awiri, 4/15

  • Tamandani Khristu, Mfumu ya Ulemerero, 2/15

  • Thandizani Ena Kuti Azichita Zonse Zimene Angathe, 6/15

  • Tikhale Oyera M’makhalidwe Athu Onse, 11/15

  • Tingatani Kuti Tikhalebe ndi Mtima Wodzipereka? 3/15

  • Tizigwirizana Kwambiri Pamene Mapeto Akuyandikira, 12/15

  • Tizikhulupirira Kwambiri Ufumu wa Mulungu, 10/15

  • Tsanzirani Chikhulupiriro cha Mose, 4/15

  • “Tsopano Ndinu Mtundu wa Anthu a Mulungu,” 11/15

  • Tumikirani Mulungu Mokhulupirika Pokumana ndi “Masautso Ambiri,” 9/15

  • Tumikirani Yehova Masiku Oipa Asanafike, 1/15

  • “Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondera Wekha,” 6/15

  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako,” 6/15

  • “Yehova Amadziwa Anthu Ake,” 7/15

  • Yehova Amaona Mavuto Athu N’kutithandiza, 4/15

  • Yehova Amatipatsa Zinthu Zofunika Ndipo Amatiteteza, 2/15

  • Yehova Ndi Mnzathu Weniweni, 2/15

  • Yehova Ndi Mulungu Wadongosolo, 5/15

  • Zimene Yehova Wachita Kuti Tiyandikane Naye, 8/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

  • Akapolo a M’madera a Ufumu wa Roma, 4/1

  • Akufa Adzaukitsidwa, 1/1

  • Aloye, 2/1

  • Amene Akulamulira Dziko, 5/1

  • Anakhalabe Wokhulupirika (Eliya), 2/1

  • Angelo, 9/1

  • Ankang’amba zovala zawo, 4/15

  • Anthu Atatu Amene Ankafufuza Choonadi m’ma 1500, 6/1

  • Chakudya Chopatsa Moyo, 6/1

  • Chifukwa Chimene Mulungu Analengera Dziko Lapansi, 6/1

  • Chipembedzo Choona, 8/1

  • Khirisimasi, 12/1

  • Kodi Anthu Ankatani kuti Sitima Zisamalowe Madzi? 7/1

  • Kodi Apitiriza Kuwononga Dzikoli N’kufika Poti Silingakonzedwenso? 9/1

  • Kodi Malamulo Amene Mulungu Anapatsa Aisiraeli Anali Achilungamo? 9/1

  • Kodi Mawu a Mulungu Amati Chiyani pa Nkhani ya Kusuta? 6/1

  • Kodi Ndibwerekedi Ndalama? 12/1

  • Kodi Pali Amene Angadziwiretu za M’tsogolo? 5/1

  • Kodi Satana Alipodi? 11/1

  • Kodi Ufumu wa Mulungu Udzakuchitirani Chiyani? 10/1

  • Kodi Ufumu wa Mulungu Unayamba Liti Kulamulira? 10/1, 11/1

  • Kodi Zipembedzo Zizichitira Zinthu Pamodzi? 3/1

  • Kugwiritsa Ntchito Gulaye pa Nkhondo, 5/1

  • Kusunga Nsomba Kuti Zisawonongeke, 7/1

  • “Kuzindikira Kumachititsa Munthu Kubweza Mkwiyo,” 12/1

  • Makolo Amene Anamwalira Adzakhalanso ndi Moyo 6/1

  • Mkazi Wamasiye wa ku Zarefati, 2/15

  • Muzilangiza Bwino Ana, 7/1

  • Mzinda wa Timgad, 12/1

  • N’chifukwa Chiyani Anthu Abwino Amakumana ndi Mavuto? 7/1

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupemphera Kuti Ufumu Ubwere? 10/1

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupemphera, Tizipemphera Bwanji? 7/1

  • N’chifukwa Chiyani Zigawenga Ankazithyola Miyendo Akamazipha? 5/1

  • ‘Ndingachitirenji Choipa Chonchi?’ (Yosefe), 11/1

  • Nkhondo Yomwe Inasintha Dziko Lonse (Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse), 2/1

  • Nsembe Zovomerezeka Pakachisi, 2/1

  • Omwe Anamwalira Adzakhalanso ndi Moyo, 1/1

  • Sanafooke Chifukwa cha Chisoni (Mariya), 5/1

  • “Tamverani Maloto” (Yosefe), 8/1

  • Thomas Emlyn, 4/1

  • Utoto Wofiira, 4/1

  • Zopereka Kukachisi wa Ayuda, 1/1

YEHOVA

  • Amadalitsa Anthu Opereka ndi Mtima Wonse, 12/15

  • Angathe Kukhala Mnzanu Wapamtima, 12/1

  • Kodi Amakuganizirani? 8/1

  • Kodi Amamva Bwanji Zinthu Zopanda Chilungamo Zikamachitika? 1/1

  • Kodi Mungaphunzitse Bwanji Ana Kumukonda? 12/1

  • Kodi Ndi Wotani? 1/1

  • Kuona Mulungu Yemwe Ndi Wosaoneka, 7/1

  • N’chifukwa Chiyani Amalola Kuti Osauka Aziponderezedwa? 2/1

  • N’chifukwa Chiyani Amalola Kuti Tizivutika? 1/1

  • Ndani Anamulenga? 8/1

  • ‘Ubwino wa Yehova’ (Sal. 27:4), 2/15

  • Zimene Wakuchitirani, 3/1

YESU KHRISTU

  • Kodi Adzachita Chiyani M’tsogolomu? 4/1

  • Kodi Akuchita Chiyani Panopa? 4/1

  • Kodi Anaukitsa Anthu? N’chifukwa Chiyani? 11/1

  • Kodi Imfa Yake Imatipindulitsa Bwanji? 3/1

  • Kodi Tizikumbukira Bwanji Imfa Yake? 3/1

  • Mwambo Womwe Simuyenera Kuuphonya (Chikumbutso), 3/1

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena