Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/99 tsamba 2
  • Mbiri Yateokalase

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mbiri Yateokalase
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
  • Nkhani Yofanana
  • Branch Letter
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • Ntchito Yapadera ku Bulgaria Inali ndi Zotsatira Zabwino
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Tidzakhala ndi Ntchito Yapadera Kuyambira pa October 16 Mpaka pa November 12
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • Mboni Zifikira Anthu mu France
    Nsanja ya Olonda—1999
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
km 2/99 tsamba 2

Mbiri Yateokalase

◼ Mboni za Yehova zinalembetsedwa mwalamulo ku Bulgaria pa October 7, 1998. Pamodzi ndi ofalitsa 946 amene ali kumeneko, tikuthokoza Yehova chifukwa cha nkhaniyi.

◼ Pa October 12, 1998, boma la Latvia linaloleza kuti mipingo yoyambirira iŵiri mwa mipingo 21 imene ili m’dzikolo ilembetse.

◼ Abale ku France akupirira pa ntchito yawo yolalikira Ufumu mosasamala kanthu za chitsutso. Mu November ndi December, ndawala yoyesa kuchititsa anthu a dzikolo kulingalira za Baibulo inalinganizidwa pa kugaŵira mwapadera bolosha la Buku la Anthu Onse. Pafupifupi anthu a pabeteli 50 a ku France asamukira ku Britain kuti akathandize ntchito yosindikiza ndi kutumiza mabuku pa nthambiyo, pamene anthu otsala 250 a banja la Beteli ya ku France ndi abale amene ali m’dzikolo akupitiriza kutumikira mwachimwemwe m’mikhalidwe yanthaŵi zonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena