Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 6
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 6
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa April 6

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 6

Nyimbo Na. 51 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 11 ndime 1-8 ndi chigawo chachiwiri patsamba 107 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 16-18 (Mph. 8)

Na. 1: 1  Samueli 18:17-24 (Osapitirira mph. 3)

Na. 2: Kodi Mulungu Ndi Amene Amachititsa Kuti Anthu Azivutika?—igw tsa. 14 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupewa Kudzikuza?—bt tsa. 81-82 ndime 17-21 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: ‘Khalani Okonzekera Ntchito Iliyonse Yabwino.’​—Tito 3:1.

Nyimbo Na. 85

Mph. 10: Zimene Munganene Pogawira Magazini a April. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita chitsanzo cha mmene tingagawirire magaziniwo pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zimene zili patsamba lino. Kenako kambiranani zitsanzo za ulalikizo kuyambira poyamba mpaka pamapeto.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Pezani Anthu Oti Muziwapatsa Magazini Mwezi Uliwonse.” Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zomwe anakumana nazo.

Mph. 10: Zofunika pampingo.

Nyimbo Na. 106 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena