Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 January tsamba 8-9
  • February 3-9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 3-9
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 January tsamba 8-9

FEBRUARY 3-9

MASALIMO 144-146

Nyimbo Na. 145 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. “Osangalala Ndi Anthu Amene Mulungu Wawo Ndi Yehova”

(10 min.)

Yehova amadalitsa anthu amene amamudalira (Sl 144:11-15; w18.04 32 ¶3-4)

Timasangalala ndi chiyembekezo chathu (Sl 146:5; w22.10 28 ¶16-17)

Anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova adzakhala osangalala mpaka kalekale (Sl 146:10; w18.01 26 ¶19-20)

Zithunzi za abale ndi alongo a misinkhu yosiyanasiyana komanso ochokera m’mayiko osiyanasiyana akusangalala.

Tikamatumikira Yehova mokhulupirika, tikhoza kukhala osangalala kwambiri ngakhale pamene tikukumana ndi mavuto

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 145:15, 16—Kodi mavesiwa akutithandiza bwanji kuona mmene tiyenera kuchitira zinthu ndi zinyama? (it-1 111 ¶9)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 144:1-15 (th phunziro 11)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Munthuyo wakuuzani kuti amaphunzira ku yunivesite. (lmd phunziro 1 mfundo 5)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Gwiritsani ntchito vidiyo yopezeka pa Zinthu Zophunzitsira. (lmd phunziro 7 mfundo 4)

6. Nkhani

(4 min.) lmd zakumapeto A mfundo 7—Mutu: Mkazi Ayenera ‘Kulemekeza Kwambiri Mwamuna Wake.’ (th phunziro 1)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 59

7. Yehova Amafuna Kuti Tizisangalala

(10 min.) Nkhani yokambirana.

Yehova ndi Mulungu wachimwemwe. (1Ti 1:11) Anatipatsa mphatso zambiri zabwino zomwe zimasonyeza kuti amatikonda komanso amafuna kuti tizisangalala. (Mla 3:12, 13) Taganizirani mphatso ziwiri izi, chakudya komanso kaphokoso kosangalatsa.

Abale ndi alongo akuotha moto. Mmodzi akuimba gitala.

Onerani VIDIYO yakuti Chilengedwe Chimasonyeza Kuti Yehova Amafuna Tizisangalala—Chakudya Chokoma Komanso Kaphokoso Kosangalatsa. Kenako funsani funso ili:

  • Kodi mphatso ya chakudya komanso kaphokoso kosangalatsa zimatitsimikizira bwanji kuti Yehova amafuna kuti tizisangalala?

Werengani Salimo 32:8. Kenako funsani funso ili:

  • Kodi kudziwa kuti Yehova amafuna kuti muzisangalala kumakuthandizani bwanji kuti muzimvera malangizo ake omwe amapereka kudzera m’Baibulo komanso gulu lake?

8. Zofunika Pampingo

(5 min.)

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 22 ¶1-6

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena