Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsamba 8
  • May 26–June 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 26–June 1
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 May tsamba 8

MAY 26–JUNE 1

MIYAMBO 15

Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Muzithandiza Ena Kukhala Osangalala

(10 min.)

Abale athu akakumana ndi mavuto aakulu, amamva ngati masiku awo onse ndi oipa (Miy 15:15)

Muzichereza anthu amene akukumana ndi mavuto (Miy 15:17; w10 11/15 31 ¶16)

“Kuyang’ana munthu ndi nkhope yachimwemwe” komanso kulankhula mawu olimbikitsa kungamuthandize kwambiri (Miy 15:23, 30, mawu a m’munsi; w18.04 23-24 ¶16-18)

Banja lachinyamata lili kunyumba kwa mlongo wachikulire ndipo akumwa limodzi tiyi.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndi ndani mumpingo wathu amene angafunike kulimbikitsidwa? Nanga ineyo ndingamuthandize bwanji?’

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 15:22—Kodi mfundo ya palembali ingatithandize bwanji kusankha mwanzeru thandizo lachipatala? (ijwbq nkhani na. 39 ¶3)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 15:1-21 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunziro 1 mfundo 5)

5. Ulendo Woyamba

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. M’pempheni kuti muziphunzira naye Baibulo. (lmd phunziro 2 mfundo 4)

6. Kuphunzitsa Anthu

(5 min.) Limbikitsani wophunzira wanu amene akutsutsidwa ndi anthu a m’banja lake. (th phunziro 4)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 155

7. Tikhoza Kukhalabe Osangalala Ngakhale Pamene Tikukumana ndi Mavuto

(15 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYO yakuti Tikhoza Kumasangalalabe Ngakhale Kuti Tikukumana ndi Zowawa, Tikuvutika ndi Njala Komanso Tikuvutika ndi Usiwa. Kenako funsani funso lotsatirali:

  • Kodi mwaphunzira chiyani kuchokera pa zimene zinachitikira anthuwa?

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 27 ¶1-9

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 100 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena