Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsamba 9
  • June 2-8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 2-8
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 May tsamba 9

JUNE 2-8

MIYAMBO 16

Nyimbo Na. 36 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Mafunso Atatu Othandiza Kusankha Zinthu Mwanzeru

(10 min.)

Kodi ndimakhulupirira kuti malangizo a Yehova akhozadi kundithandiza? (Miy 16:3, 20; w14 1/15 19-20 ¶11-12)

Kodi zomwe ndasankhazi zisangalatsa Yehova? (Miy 16:7)

Kodi ndatengeka maganizo chifukwa cha zomwe ena akulankhula kapena kuchita? (Miy 16:25; w13 9/15 17 ¶1-3)

M’bale wachinyamata ali mushopu ndipo wogulitsa akumuonetsa suti yothina. Koma m’baleyo wasankha suti ina imene ingamukwane bwino.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi mafunso amenewa angandithandize bwanji kusankha zinthu mwanzeru pa nkhani ya zovala ndi kudzikongoletsa?’

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 16:22—Kodi “zitsiru zimalangidwa ndi kupusa kwawo komwe” m’njira yotani? (it-1 629)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 16:1-20 (th phunziro 12)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Musonyezeni mmene webusaiti ya jw.org ingamuthandizire. (lmd phunziro 2 mfundo 5)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pemphani munthu amene anakanapo kuphunzira Baibulo m’mbuyomu kuti muziphunzira naye. (lmd phunziro 9 mfundo 5)

6. Nkhani

(5 min.) ijwbv nkhani na. 40—Mutu: Kodi Lemba la Miyambo 16:3 Limatanthauza Chiyani? (th phunziro 8)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 32

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 27 ¶10-18

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 68 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena