DECEMBER 15-21
YESAYA 9-10
Nyimbo Na. 77 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Analosera za “Kuwala Kwakukulu”
(10 min.)
“Kuwala kwakukulu” kunali koti kudzaonekera ku Galileya (Yes 9:1, 2; Mt 4:12-16; ip-1 125-126 ¶16-17)
Mtundu umene udzalandire kuwalako udzakula kwambiri komanso anthu ake adzakhala osangalala (Yes 9:3; ip-1 126-128 ¶18-19)
Zotsatira za kuwala kwakukulu kumeneko zidzakhalapo mpaka kalekale (Yes 9:4, 5; ip-1 128-129 ¶20-21)
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
Yes 9:6—Kodi Yesu anasonyeza bwanji kuti anali “Mlangizi Wodabwitsa”? (ip-1 130 ¶23-24)
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Yes 10:1-14 (th phunziro 11)
4. Ulendo Woyamba
(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Lalikirani munthu amene si Mkhristu. (lmd phunziro 1 mfundo 4)
5. Ulendo Wobwereza
(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pitirizani kukambirana pogwiritsa ntchito kapepala kamene munamusiyira pa ulendo wapita. (lmd phunziro 9 mfundo 3)
6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira
(5 min.) Chitsanzo. Ijwfq nkhani Na. 35—Mutu: Kodi a Mboni za Yehova Anasintha Zina N’zina M’Baibulo Kuti Zigwirizane ndi Zimene Amakhulupirira? (th phunziro 12)
Nyimbo Na. 95
7. Kuwala Kukuwonjezerekabe
(5 min.) Nkhani yokambirana.
Gulu la Yehova likupitiriza kupita patsogolo. Kodi mukuyenda nalo limodzi? Tiyeni tikambirane zinthu zitatu zosonyeza mmene gulu la Yehova lakhala likuyendera komanso mmene zimenezo zatithandizira.
Lembani chitsanzo chosonyeza kusintha kwa mmene tinkamvera mfundo inayake yachoonadi cha m’Baibulo komanso mmene kusinthako kwatithandizira.—Miy 4:18
Lembani chitsanzo chosonyeza kusintha pa nkhani ya mmene timagwirira ntchito yolalikira komanso mmene kusinthako kwatithandizira kukwaniritsa ntchito imene Yesu anatipatsa.—Mt 28:19, 20
Lembani chitsanzo chosonyeza kusintha komwe kwachitika pa nkhani ya mmene zinthu zimayendera m’gululi komanso mmene kusinthako kwatithandizira.—Yes 60:17
8. Vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya December
(10 min.)
9. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) lfb mawu oyamba gawo 8 komanso mutu 44-45