Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 202-203
  • Mawu Oyamba Gawo 13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 13
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Oyamba Gawo 11
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Mawu Oyamba Gawo 12
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Mawu Oyamba Gawo 3
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Mawu Oyamba Gawo 1
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 202-203
Yesu akusambitsa mapazi a atumwi ake

Mawu Oyamba Gawo 13

Yesu anabwera padzikoli kudzafera anthu ochimwa. Ngakhale kuti anafa, iye anagonjetsa dziko. Yehova anachita zinthu mokhulupirika ndipo anaukitsa Mwana wakeyu. Nthawi yonse imene Yesu anali padzikoli, anali wodzichepetsa, ankatumikira anthu ndipo anthuwo akalakwitsa ankawakhululukira. Yesu ataukitsidwa anapita kukaonana ndi ophunzira ake. Iye anawaphunzitsa mmene angagwirire ntchito yofunika kwambiri imene anawapatsa. Ngati ndinu kholo thandizani mwana wanu kudziwa kuti nafenso tiyenera kugwira ntchito imeneyi.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Palibe vuto limene Yehova angalephere kulithetsa

  • Tizitumikira ena komanso kuwathandiza ngati mmene Yesu ankachitira

  • Akhristu enieni amadziwika chifukwa choti amakondana

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena