Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm19 tsamba 6-7
  • Lamlungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lamlungu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MASANA
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
CO-pgm19 tsamba 6-7

Lamlungu

“PITIRIZANI KUCHITA ZINTHU ZIMENE ZINGACHITITSE MULUNGU KUKUKONDANI”​—YUDA 21

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 106 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Muzikumbukira Zimene Chikondi Chimachita Komanso Zimene Sichichita

    • N’choleza Mtima Ndiponso N’chokoma Mtima (1 Akorinto 13:4)

    • Sichichita Nsanje, Sichidzitama (1 Akorinto 13:4)

    • Sichidzikuza, Sichichita Zosayenera (1 Akorinto 13:4, 5)

    • Sichisamala Zofuna Zake Zokha, Sichikwiya (1 Akorinto 13:5)

    • Sichisunga Zifukwa, Sichikondwera ndi Zosalungama (1 Akorinto 13:5, 6)

    • Chimakondwera ndi Choonadi, Chimakwirira Zinthu Zonse (1 Akorinto 13:6, 7)

    • Chimakhulupirira Zinthu Zonse, Chimayembekezera Zinthu Zonse (1 Akorinto 13: 7)

    • Chimapirira Zinthu Zonse, Chikondi Sichitha (1 Akorinto 13:7, 8)

  • 11:10 Nyimbo Na. 150 ndi Zilengezo

  • 11:20 NKHANI YA ONSE: Kodi Mungapeze Kuti Chikondi Chenicheni M’dziko la Anthu Opanda Chikondili? (Yohane 13:34, 35)

  • 11:50 Phunziro Lachidule la Nsanja ya Olonda

  • 12:20 Nyimbo Na. 1 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 124

  • 1:50 VIDIYO: Nkhani ya Yosiya Imatiphunzitsa Kukonda Yehova Komanso Kudana ndi Zoipa​—Mbali Yachiwiri (2 Mafumu 22:3-20; 23:1-25; 2 Mbiri 34:3-33; 35:1-19)

  • 2:20 Nyimbo, “Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima” Komanso Zilengezo

  • 2:30 Muzichita Chidwi Ndi Ntchito za Yehova Zosonyeza Chikondi Chokhulupirika (Salimo 107:43; Aefeso 5:1, 2)

  • 3:30 Nyimbo Yatsopano Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena