Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 42
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tikukuthokozani Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikuyamikani, Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Dzina Lanu Ndi Yehova’
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 42

NYIMBO 42

Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Losindikizidwa

(Aefeso 6:18)

  1. 1. M’lungu Atate Wamphamvuyonse,

    Dzina lanu liziyeretsedwadi.

    Mumachita zomwe mwafuna.

    Tikupempha Ufumu ubwere.

    Pa nthawi yanu M’lungu

    Mudzatidalitsatu.

  2. 2. Mumatipatsa zinthu zabwino,

    Mphatso zoti sitikanazipeza.

    Mumatipatsatu kuwala

    Ndipo mumatipatsanso nzeru.

    Tikukuthokozani

    Ndinudi wachikondi.

  3. 3. Mavuto ndi ambiri m’dzikoli.

    Tikupempha muzititonthozabe.

    Tikuuzeni nkhawa zathu,

    Muzitithandiza kupirira

    Komanso kukwanitsa

    Zomwe tinalonjeza.

(Onaninso Sal. 36:9; 50:14; Yoh. 16:33; Yak. 1:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena