Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 46
  • Tikukuthokozani Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikukuthokozani Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tikuyamikani, Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Umakumbukira Kunena Kuti Zikomo?
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 46

NYIMBO 46

Tikukuthokozani Yehova

Losindikizidwa

(1 Atesalonika 5:​18)

  1. 1. Tikukuthokozanitu Yehova.

    Mumatipatsa kuwala kwanu.

    Tikuthokoza mwayi wa pemphero

    Kuti tinene mavuto athu.

  2. 2. Tikuthokoza potumiza Yesu

    Amene anagonjetsa dziko.

    Tikuthokozanso potithandiza

    Kukwanitsa malonjezo athu.

  3. 3. Tikuthokoza chifukwa cha mwayi

    Wolalikira za dzina lanu.

    Tikuthokoza kuti posachedwa

    Mavuto onsewa adzathadi.

(Onaninso Sal. 50:14; 95:2; 147:7; Akol. 3:​15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena