Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 43
  • Pemphero Lothokoza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pemphero Lothokoza
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Khalani Akuyamika”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • Pemphero Loyamikira
    Imbirani Yehova
  • “Sonyezani Kuti Ndinu Oyamikira”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
  • “Muziyamika pa Chilichonse”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 43

NYIMBO 43

Pemphero Lothokoza

Losindikizidwa

(Salimo 95:2)

  1. 1. Yehova tikufuna kuthokoza

    Kudzera mupemphero lathuli.

    Tizitumikira mofunitsitsa,

    Timadziwa mumatithandiza.

    Ndife anthu obadwa ndi uchimo

    Chonde muzitikhululukira.

    Tikuthokoza munatiwombola

    Ndi dipo la mwana wanu Yesu.

  2. 2. Zikomo chifukwa munatikonda,

    Munatikokeranso kwa inu.

    Tiphunzitseni za inu Mulungu

    Kuti nafe tizikukondani.

    Zikomo chifukwa cha mzimu wanu,

    Timalankhula molimba mtima.

    Tizitumikira modzichepetsa.

    Tikukuthokozani Yehova.

(Onaninso Sal. 65:​2, 4, 11; Afil. 4:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena